Joshua 21:40 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero mabanja a Merari, adapatsidwa mizinda khumi ndi iŵiri mwamaere.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yonseyi ndiyo midzi ya ana a Merari monga mwa mabanja ao, ndiwo otsala a mabanja a Alevi; ndipo gawo lao ndilo midzi khumi ndi iwiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho mabanja onse a Merari, amene anali otsala a fuko la Levi analandira mizinda khumi ndi iwiri pogwiritsa ntchito maere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yonseyi ndiyo midzi ya ana a Merari monga mwa mabanja ao, ndiwo otsala a mabanja a Alevi; ndipo gawo lao ndilo midzi khumi ndi iwiri.