Joshua 21:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mabanja a Merari adapatsidwa mizinda 12, kuchokera m'mafuko a Rubeni, Gadi ndi Zebuloni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ana a Merari, monga mwa mabanja ao, analandira motapa pa fuko la Rubeni, ndi pa fuko la Gadi, ndi pa fuko la Zebuloni midzi khumi ndi iwiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mabanja a Merari anapatsidwa mizinda khumi ndi iwiri kuchokera ku mafuko a Rubeni, Gadi ndi Zebuloni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ana a Merari, monga mwa mabanja ao, analandira motapa pa pfuko la Rubeni, ndi pa pfuko la Gadi, ndi pa pfuko la Zebuloni midzi khumi ndi iwiri.