Joshua 9:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tangoonani bulediyu. Pochoka kwathu, buledi ameneyu anali wofunda ndithu, koma tangoonani ali gwaa ndiponso wochita chuku.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mkate wathu uwu tinadzitengera kamba m'nyumba zathu, ukali wamoto, tsiku lotuluka ife kudza kwanu kuno; koma tsopano, taonani uli wouma ndi woyanga nkhungu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Buledi wathuyu anali wotentha pamene timanyamuka ku mudzi kubwera kwa inu. Koma tsopano taonani ali gwaa ndiponso wawola.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mkate wathu uwu tinadzitengera kamba m'nyumba zathu, ukali wamoto, tsiku loturuka Ife kudza kwanu kuno; koma tsopano, taonani, uli wouma ndi woyaoga nkhungu;