Joshua 9:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Popeza kuti mwachita zimenezi, Mulungu wakutembererani. Nthaŵi zonse inu ndiye muzidzatidulira nkhuni, ndi kutitungira madzi ku Nyumba ya Mulungu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo tsopano mukhale otembereredwa, palibe mmodzi wa inu adzamasuka wosakhala kapolo, ndi kutemera nkhuni, ndi kutungira madzi nyumba ya Mulungu wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsopano popeza mwachita izi, Mulungu wakutembererani ndipo palibe wina mwa inu amene akhale mfulu. Nthawi zonse inu muzidzatidulira nkhuni ndi kutitungira madzi ku Nyumba ya Yehova.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo tsopano mukhale otembereredwa, palibe mmodzi wa inu adzamasuka wosakhala kapolo, ndi kutemera nkhuni, ndi kutungira madzi nyumba ya Mulungu wanga.