Judges 11:37 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iye adamuuzanso bambo wakeyo kuti, “Mundichitire ichi chokha. Bandilekani miyezi iŵiri ndizikayendayenda ku mapiri, kuti ndizikalira pamodzi ndi anzanga kuti ndikufa ndili namwali.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anati kwa atate wake, Andichitire ichi, andileke miyezi iwiri, kuti ndichoke ndi kutsikira kumapiri, ndi kulirira unamwali wanga, ine ndi anzanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anatinso kwa abambo ake, “Ndikupempheni chinthu ichi: Mundilole ndikayendeyende ku mapiri miyezi iwiri ndizikalira pamodzi ndi anzanga chifukwa ndikufa ndikanali namwali wosadziwa mwamuna.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anati kwa atate wace, Andicitire ici, andileke miyezi iwiri, kuti ndicoke ndi kutsikira kumapiri, ndi kulirira unamwali wanga, ine ndi anzanga.