Judges 12:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo Abidoniyo adamwalira, naikidwa ku Piratoni m'dziko la Efuremu, ku mapiri a Aamaleke.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nafa Abidoni mwana wa Hilele wa ku Piratoni, naikidwa m'Piratoni m'dziko la Efuremu ku mapiri a Amaleke.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Abidoni mwana wa Hilelo Mpiratoni uja anamwalira, nayikidwa ku Piratoni, mʼdziko la Efereimu, dziko lamapiri la Aamaleki.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nafa Abidoni mwana wa Hilele wa ku Piratoni, naikidwa m'Piratoni m'dziko la Efraimu ku mapiri a Amaleki.