Judges 13:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mngelo wa Chautayo adafunsa Manowa kuti, “Chifukwa chiyani mukufuna kudziŵa dzina langa? Dzina laketu nlodabwitsa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mthenga wa Yehova anati kwa iye, Ufunsiranji dzina langa, popeza lili lodabwitsa?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anayankha kuti, “Nʼchifukwa chiyani mukufunsa dzina langa? Dzina laketu ndi lodabwitsa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mthenga wa Yehova anati kwa iye, Ufunsiranji dzina langa, popeza liri lodabwitsa?