Judges 13:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero mkaziyo adabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Samisoni. Mnyamatayo adakula ndipo Chauta adamdalitsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mkaziyo anabala mwana wamwamuna namutcha dzina lake Samisoni; nakula mwanayo, Yehova namdalitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Motero mkaziyo anabereka mwana wa mwamuna, namutcha dzina lake Samsoni. Iye anakula ndipo Yehova anamudalitsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mkaziyo anabala mwana wamwamuna namucha dzina lace Samsoni; nakula mwanayo, Yehova namdalitsa.