Judges 13:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo Mzimu wa Chauta udayamba kumlimbitsa pamene anali ku zithando za anthu a fuko la Dani, pakati pa Zora ndi Esitaoli.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mzimu wa Yehova unayamba kumfulumiza mtima ku misasa ya Dani pakati pa Zora ndi Esitaoli.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mzimu wa Yehova unayamba kumulimbikitsa pamene ankakhala ku misasa ya anthu a fuko la Dani, malo amene anali pakati pa Zora ndi Esitaoli.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mzimu wa Yehova unayamba kumfulumiza mtima ku misasa ya Dani pakati pa Zora ndi Esitaoli.