Judges 16:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Delila adauza Samisoni kuti, “Inu, tandiwuzani, kodi mphamvu zanu zoopsazi zagona poti? Kodi munthu atati akumangeni kuti akugonjetseni, nkofunika kuti atani?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo Delila anati kwa Samisoni, Ndikupempha, undiuze umo muchokera mphamvu yako yaikulu, ndi chimene angakumange nacho, kuti akuzunze.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho Delila anati kwa Samsoni, “Inu tandiwuzani pamene pagona mphamvu zanu zoopsazi ndi mmene anthu akhoza kukumangirani kuti akugonjetseni.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo Delila anati kwa Samsoni, Ndikupempha, undiuze umo mucokera mphamvu yako yaikuru, ndi cimene angakumange naco, kuti akuzunze.