Judges 17:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Mika adalonga Mleviyo unsembe, ndipo iyeyo ankakhala m'nyumba mwa Mika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Mika anamninkha zansembe Mleviyo, ndi mnyamatayo anakhala wansembe wake, nakhala m'nyumba ya Mika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pambuyo pake Mika anapatula Mleviyo ndipo mnyamatayu anakhala wansembe. Tsono ankakhala mʼnyumba ya Mika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Mika anamninkha zansembe Mleviyo, ndi mnyamatayo anakhala wansembe wace, nakhala m'nyumba ya Mika.