Judges 17:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ku Betelehemu m'dziko la Yuda kunali mnyamata wina wa fuko la Yuda amene anali Mlevi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panali mnyamata wa ku Betelehemu-Yuda wa banja la Yuda, ndiye Mlevi, nagonera iye komweko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ku Betelehemu mʼdziko la Yuda kunali mnyamata wina amene anali wa fuko la Levi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panali mnyamata wa ku Betelehemu-Yuda wa banja la Yuda, ndiye Mlevi, nagonera iye komweko.