Judges 20:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atsogoleri a anthu onse ndi a mafuko onse a Aisraele adabwera ku msonkhano wa anthu a Mulungu. Onse pamodzi analipo 400,000 oyenda pansi omenya nkhondo ndi lupanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo akulu a anthu onse a mafuko onse a Israele anadziimika mu msonkhano wa anthu a Mulungu, anthu oyenda pansi zikwi mazana anai akusolola lupanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atsogoleri a anthu onse ndi a mafuko onse Aisraeli anali nawo pa msonkhano wa anthu a Mulungu. Onse pamodzi analipo asilikali oyenda pansi 400,000 atanyamula malupanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo akuru a anthu onse a mapfuko onse a Israyeli anadziimika mu msonkhano wa anthu a Mulungu, anthu oyenda pansi zikwi mazana anai akusolola lupanga,