Judges 21:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Aisraele anali atalumbira ku Mizipa kuti, “Palibe ndi mmodzi yemwe mwa ife amene adzapereke mwana wake wamkazi kuti akwatiwe ndi Abenjamini.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma amuna a Israele adalumbira ku Mizipa, ndi kuti, Palibe mmodzi wa ife adzapereka mwana wake wamkazi kwa Mbenjamini akhale mkazi wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Aisraeli anali atalumbira ku Mizipa kuti, “Palibe mmodzi wa ife adzapereke mwana wake wamkazi kuti akwatiwe ndi mwamuna wa fuko la Benjamini.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma amuna a Israyeli adalumbira ku Mizipa, ndi kuti, Palibe mmodzi wa ife adzapereka mwana wace wamkazi kwa Mbenjamini akhale mkazi wace.