Judges 21:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo mpingo wonse udatumiza uthenga kwa Abenjamini amene anali ku thanthwe la ku Rimoni kukaŵauza kuti nkhondo yatha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo msonkhano wonse unatumiza mau kwa ana a Benjamini okhala m'thanthwe la Rimoni, nawalalikira mtendere.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kenaka msonkhano wonse unatumiza uthenga kwa Abenjamini amene ankakhala ku thanthwe la Rimoni kuwawuza kuti nkhondo yatha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo msonkhano wonse unatumiza mau kwa ana a Benjamini okhala m'thanthwe la Rimoni, nawalalikira mtendere.