Judges 21:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndiye adalamula Abenjamini aja kuti, “Pitani mukabisale m'minda yamphesa,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo analamulira ana a Benjamini ndi kuti, Mukani, mulalire m'minda yamphesa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho anawalamulira Abenjamini aja kuti, “Pitani mukabisale mʼminda ya mpesa
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo analamulira ana a Benjamini ndi kuti, Mukani, mulalire m'minda yamphesa;