Judges 21:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi tidzaŵapezera kuti akazi anthu amene atsaliraŵa, popeza kuti talumbira kwa Chauta kuti sitidzaŵapatsa ana athu aakazi kuti aŵakwatire?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tidzatani kuwafunira otsalawo akazi, popeza tinalumbira ife pa Yehova kuti sitidzawapatsa ana athu akazi akhale akazi ao?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi tingawapezere bwanji anthu otsalawa akazi woti awakwatire? Paja ife tinalumbira kwa Yehova kuti sitidzapereka ana anthu aakazi kuti awakwatire.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tidzatani kuwafunira otsalawo akazi, popeza tinalumbira ife pa Yehova kuti sitidzawapatsa ana athu akazi akhale akazi ao?