Judges 3:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Ehudi adasula lupanga lake lakuthwa kuŵiri, kutalika kwake masentimita 50. Ndipo adamangirira lupangalo pa ntchafu yake yakumanja m'kati mwa zovala zake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Ehudi anadzisulira lupanga lakuthwa konsekonse utali wake mkono; nalimangirira pansi pa zovala zake pa ntchafu ya kulamanja.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Ehudi anapanga lupanga lakuthwa kuwiri lotalika masentimita makumi asanu, ndipo anamangirira lupangalo pa ntchafu yake ya kumanja mʼkati mwa zovala zake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Ehudi anadzisulira lupanga lakuthwa konse konse utali wace mkono; nalimangirira pansi pa zobvala zace pa ncafu ya kulamanja.