Judges 6:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Chauta adamuuza kuti, “Mtendere ukhale nawe. Usaope, suufa,”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova anati kwa iye, Mtendere ukhale ndi iwe, usaope, sudzafa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Yehova anamuwuza kuti, “Mtendere ukhale ndi iwe! Usachite mantha, sufa ayi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova anati kwa iye, Mtendere ukhale ndi iwe, usaope, sudzafa.