Judges 9:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma mkuyuwo udalandula, udati, ‘Ine sindingasiye zipatso zanga zokomazi nkuzuna kwakeku, kuti ndizikalamulira mitengo.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mkuyu unanena nao, Ngati ndidzasiya kuzuna kwanga, ndi zipatso zanga zokoma kukalenga pa mitengo?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma mtengo wa mkuyu unayankha kuti, “Kodi ndisiye chipatso changa chokoma ndi chozunachi kuti ndizikalamulira mitengo?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mkuyu unanena nao, Ngati ndidzasiya kuzuna kwanga, ndi zipatso zanga zokoma kukalenga pa mitengo?