Judges 9:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma mtengo wamphesawo udalandula, udati, ‘Ine sindingasiye kupereka vinyo amene amasangalatsa milungu ndi anthu omwe, kuti ndizikalamulira mitengo.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mpesa unanena nao, Ngati ndidzasiya vinyo wanga wakusekeretsa Mulungu ndi anthu, kukalenga pa mitengo?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma mtengo wamphesa unayankha kuti, “Kodi ine ndisiye vinyo wangayu, amene amasangalatsa milungu ndi anthu omwe kuti ndizikalamulira mitengo?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mpesa unanena nao, Ngati ndidzasiya vinyo wanga wakusekeretsa Mulungu ndi anthu, kukalenga pa mitengo?