Lamentations 3:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndasanduka chinthu chomachiseka, kwa anthu a mitundu ina, amandiimba nyimbo zondinyoza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndasanduka wondiseka mtundu wanga wonse, ndi nyimbo yao tsiku lonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndinakhala choseketsa cha anthu anga onse; amandinyodola mʼnyimbo zawo tsiku lonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndasanduka wondiseka mtundu wanga wonse, ndi nyimbo yao tsiku lonse.