Lamentations 3:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho ndikuti, “Ulemerero wanga wonse watha, chandithera chikhulupiriro cholandira kanthu ka Chauta.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinati, Mphamvu yanga yatha, osayembekezanso kanthu kwa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho ndikuti, “Ulemerero wanga wachoka ndi zonse zimene ndimayembekeza kwa Yehova.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinati, Mphamvu yanga yatha, osayembekezanso kanthu kwa Yehova.