Lamentations 3:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nthaŵi zonse ndimangozilingalirabe zimenezi, nkuwona ndataya mtima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Moyo wanga uzikumbukirabe nuwerama mwa ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndikuzikumbukira bwino izi, ndipo moyo wanga wathedwa mʼkati mwanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Moyo wanga uzikumbukirabe nuwerama mwa ine,