Lamentations 3:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nkwabwinonso kuti munthu asenze goli la kupirira pamene iye ali pa unyamata.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nkokoma kuti munthu asenze goli ali wamng'ono.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nʼkwabwino kuti munthu asenze goli pamene ali wamngʼono.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nkokoma kuti munthu asenze gori ali wamng'ono.