Lamentations 3:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Angathe kulanga mwankhalwe, komabe adzaonetsa chifundo, chifukwa chikondi chao nchochuluka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Angakhale aliritsa, koma adzachitira chisoni monga mwa kuchuluka kwa zifundo zake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo, chifukwa chikondi chake ndi chosatha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Angakhale aliritsa, koma adzacitira cisoni monga mwa kucuruka kwa zifundo zace.