Lamentations 3:34 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta amadziŵa pamene akulu amapondereza am'ndende am'dziko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kupondereza andende onse a m'dziko,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuphwanya ndi phazi a mʼndende onse a mʼdziko,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kupondereza andende onse a m'dziko,