Lamentations 3:50 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
mpaka Chauta adzayang'ane pansi kuchokera kumwamba ndi kuwona mavuto anga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kufikira Yehova adzazolika kumwamba ndi kuona.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
mpaka Yehova ayangʼane pansi kuchokera kumwamba ndi kuona.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kufikira Yehova adzazolika kumwamba ndi kuona;