Lamentations 4:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngakhale akazi achifundo ndi manja ao omwe adafika pophika ana ao. Ana aowo adasanduka chakudya chao pa nthaŵi imene anthu anga adaonongedwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Manja a akazi achisoni anaphika ana aoao; anali chakudya chao poonongeka mwana wamkazi wa anthu a mtundu wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amayi achifundo afika pophika ana awo enieni, ndiwo anali chakudya chawo pamene anthu anga anali kuwonongeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Manja a akazi acisoni anaphika anaanao; Anali cakudya cao poonongeka mwana wamkazi wa anthu a mtundu wanga.