Lamentations 5:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kaya, monga nkuti mwatitayiratu? Monga nkuti mwatikwiyira kopitirira?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mwatikaniza konse, mwatikwiyira kopambana.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pokhapokha ngati mwatitaya kotheratu, ndi kuti mwatikwiyira kobzola muyeso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mwatikaniza konse, Mwatikwiyira kopambana.