Leviticus 13:40 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Tsitsi la munthu likatha kumutu chapankhongo, ndiye kuti ndi dazi limenelo, koma munthuyo ndi wosaipitsidwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ngati tsitsi la munthu lathothoka, ndiye wadazi; koma woyera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tsitsi la munthu likayoyoka kumutu ndiye kuti ndi dazi limenelo koma munthuyo ndi woyeretsedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ngati tsitsi la munthu lathothoka, ndiye wadazi; koma woyera.