Leviticus 14:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wansembe atenge mwanawankhosa woperekera nsembe yopepesera kupalamula, pamodzi ndi mafuta aja, ndipo aziweyule, kuti zikhale zopereka zoweyula pamaso pa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo wansembe atenge mwanawankhosa wa nsembe yopalamula, ndi muyeso uja wa mafuta, ndipo wansembe aziweyula nsembe yoweyula pamaso pa Yehova;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Wansembe atenge mwana wankhosa wopereka nsembe yopepesera kupalamula, pamodzi ndi mafuta aja, ndipo aziweyule kuti zikhale nsembe yoweyula pamaso pa Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo wansembe atenge mwana wa nkhosa wa nsembe yoparamula, ndi muyeso wa mafuta, ndipo wansembe aziweyule nsembe yoweyula pamaso pa Yehova;