Leviticus 14:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
awazeko mafutawo kasanu ndi kaŵiri ndi chala cha ku dzanja lamanja pamaso pa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo wansembe awazeko mafuta aja ali m'dzanja lake lamanzere ndi chala chake cha dzanja lamanja, kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo ndi chala chake cha ku dzanja lamanja awaze mafutawo kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo wansembe awazeko mafuta aja ali m'dzanja lace lamanzere ndi cala cace ca dzanja lamanja, kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova;