Leviticus 14:35 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
mwiniwake nyumbayo adzapite kwa wansembe, akamuuze kuti, ‘Ndikuwona ngati kuti m'nyumba mwanga muli ndere.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pamenepo mwini nyumbayo adzauze wansembe, kuti, Ndiyesa muli ngati nthenda m'nyumba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
mwini wake nyumbayo adzapite kwa wansembe ndi kukamuwuza kuti, ‘Ndaona chinthu chooneka ngati ndere mʼnyumba mwanga.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pamenepo mwini nyumbayo adzauze wansembe, kuti, Ndiyesa muli ngati nthenda m'nyumba.