Leviticus 15:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwamuna akataya mbeu yake pogona ndi mkazi, onse aŵiriwo asambe, koma akhalabe oipitsidwa mpaka madzulo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mkazi yemwe, mwamuna atagona naye, onse awiri asambe ndi madzi, nadzakhala odetsedwa kufikira madzulo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwamuna akagona ndi mkazi wake nataya mbewu yake yaumuna, onse awiriwo asambe. Komabe adzakhala odetsedwa mpaka madzulo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mkazi yemwe, mwamuna atagona naye, onse awiri asambe ndi madzi, nadzakhala odetsedwa kufikira madzulo.