Leviticus 18:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usagone ndi mwamuna ngati mkazi. Chimenecho ndi chinthu chonyansa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usamagonana ndi mwamuna, monga amagonana ndi mkazi; chonyansa ichi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“ ‘Usagonane ndi mwamuna ngati mkazi; chimenecho ndi chinthu chonyansa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usamagonana ndi mwamuna, monga amagonana ndi mkazi; conyansa ici.