Leviticus 18:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Musachite zimenezi kuti dziko lingakusanzeni mukaliipitsa, monga momwe lidasanzira mtundu wa anthu umene udaalipo m'dzikomo, inu musanafike.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
lingakusanzeni inunso dzikoli, polidetsa inu, monga linasanza mtundu wa anthu wokhalako musanafike inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma inu musachite zimenezi kuti dziko lingakusanzeni mutaliyipitsa monga linasanzira mitundu imene imakhalamo inu musanafike.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
lingakusanzeni inunso dzikoli, polidetsa inu, monga linasanza mtundu wa anthu wokhalako musanafike inu.