Leviticus 21:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma angathe kudya chakudya choperekedwa kwa Mulungu wake, buledi wopatulika kopambana uja, pamodzi ndi zotsalira zopatulika za nsembe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Adye chakudya cha Mulungu wake, chopatulika kwambiri, ndi chopatulika;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma iye angathe kudya chakudya chopatulika kwambiri chija, ngakhalenso chakudya chotsala pa nsembe zopatulika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Adye cakudya ca Mulungu wace, copatulikitsa, ndi copatulika;