Leviticus 24:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsiku lina munthu wina amene mai wake anali Wachiisraele, koma bambo wake anali wa ku Ejipito, adapita kwa Aisraele ndipo adakangana ndi Mwisraele mmodzi ku mahema.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mwana wamwamuna wa mkazi Wachiisraele, atate wake ndiye Mwejipito, anatuluka mwa ana a Israele; ndi mwana wamwamuna wa mkazi Wachiisraeleyo analimbana naye munthu Mwisraele kuchigono;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsiku lina munthu wina wamwamuna amene amayi ake anali Mwisraeli koma abambo ake anali Mwigupto anapita kwa Aisraeli ndipo anakangana ndi Mwisraeli wina ku msasa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mwana wamwamuna wa mkazi M-israyeli, atate wace ndiye M-aigupto, anaturuka mwa ana a Israyeli; ndi mwana wamwamuna wa mkazi M-israyeliyo analimbana naye munthu M-israyeli kucigono;