Leviticus 24:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pa mzere uliwonse muikepo lubani wokoma, kuti pamodzi ndi bulediyo akhale chikumbutso cha nsembe yopsereza yopereka kwa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nuike lubani loona ku mzere uliwonse, kuti likhale kumkate ngati chokumbutsa, nsembe yamoto ya Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pa mzere uliwonse muyikepo lubani wafungo lokoma kuti pamodzi ndi bulediyo akhale wachikumbutso cha nsembe yopsereza yopereka kwa Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nuike libano loona ku mzere uli wonse, kuti likhale kumkate ngati cokumbutsa, nsembe yamoto ya Yehova.