Leviticus 25:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene mubzala pa chaka chachisanu ndi chitatu muzidzadya sundwe. Mpaka chaka chachisanu ndi chinai pokolola, mudzidzadyabe sundwe.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mubzale chaka chachisanu ndi chitatu, ndi kudya zipatso zasundwe; kufikira chaka chachisanu ndi chinai, mpaka zitacha zipatso zake mudzadya zasundwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene mukudzala chaka chachisanu ndi chitatu, muzidzadya chakudya chogonera ndipo mudzapitirira kudya mpaka nthawi yokolola mʼchaka chachisanu ndi chinayi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mubzale caka cacisanu ndi citatu, ndi kudya zipatso zasundwe; kufikira caka cacisanu ndi cinai, mpaka zitacha zipatso zace mudzadya zasundwe.