Leviticus 26:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mudzadya ana anu aamuna, ndipo mudzadyanso ana anu aakazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mudzadya nyama ya ana anu amuna; inde nyama ya ana anu akazi mudzaidya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mudzadya ana anu aamuna ndiponso mudzadya ana anu aakazi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mudzadya nyama ya ana anu amuna; inde nyama ya ana anu akazi mudzaidya.