Leviticus 26:38 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mudzatha, kuchita kuti psiti, pakati pa mitundu ya anthu, ndipo dziko la adani anu lidzakudyani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mudzatayika mwa amitundu, ndi dziko la adani anu lidzakudyani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mudzatheratu pakati pa mitundu ya anthu. Dziko la adani anu lidzakudyani.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mudzatayika mwa amitundu, ndi dziko la adani anu lidzakudyani.