Leviticus 27:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ngati safuna kuti aombole kapena ngati waugulitsa kwa munthu wina, mundawo sudzaombolekanso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma akapanda kuombola mundawo, kapena atagulitsa mundawo kwa munthu wina, suomboledwanso;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngati sawuwombola mundawo, kapena ngati waugulitsa kwa munthu wina, mundawo sudzawomboledwanso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma akapanda kuombola mundawo, kapena atagulitsa mundawo kwa munthu wina, suomboledwanso;