Leviticus 27:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Koma pasakhale munthu amene apereke mwana woyamba wa nyama. Mwanayo ali kale wa Chauta, popeza kuti ndi woyamba. Ngakhale ikhale ng'ombe kapena nkhosa, nja Chauta imeneyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Komatu woyamba kubadwa mwa nyama akhale wobadwa woyamba wa Yehova, munthu asampatule; ingakhale ng'ombe ingakhale nkhosa, ndiye wa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“ ‘Koma pasapezeke munthu wopereka mwana woyamba kubadwa wa nyama, popeza mwana woyamba kubadwa ali kale wa Yehova, kaya ndi ngʼombe kapena nkhosa, zimenezi ndi za Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Komatu woyamba kubadwa mwa nyama akhale wobadwa woyamba wa Yehova, munthu asampatule; ingakhale ng'ombe ingakhale nkhosa, ndiye wa Yehova.