Leviticus 27:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu akafuna kuti aombole chigawo chimodzi chachikhumi chilichonse, aonjezepo chimodzi mwa zigawo zisanu za mtengo wake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma munthu akaombolatu kanthu ka limodzi la magawo khumiwo aonjezeko limodzi la magawo asanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati munthu afuna kuwombola chakhumi chilichonse, awonjezere pamtengo wake chimodzi mwa zigawo zisanu za mtengowo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma munthu akaombolatu kanthu ka limodzi la magawo khumiwo aonjezeko limodzi la magawo asanu.