Leviticus 27:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wake akakhala wamkazi, mtengo wake ukhale wokwana masekeli asiliva makumi atatu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma akakhala wamkazi, umuyesere wa masekeli makumi atatu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo ngati ndi wamkazi, mtengo wake ukhale masekeli makumi atatu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma akakhala wamkazi, umuyesere wa masekeli makumi atatu.