Leviticus 27:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Akakhala munthu wa zaka zisanu mpaka zaka makumi aŵiri, mtengo wake ukhale wokwana masekeli asiliva makumi aŵiri pa munthu wamwamuna, ndipo khumi pa munthu wamkazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akakhala munthu wa zaka zisanu kufikira wina wa zaka makumi awiri uwayesere, wamwamuna wa masekeli makumi awiri, ndi wamkazi wa masekeli khumi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mtengo wa munthu wamwamuna wa zaka zapakati pa zisanu ndi makumi awiri ukhale masekeli makumi awiri ndipo munthu wamkazi ukhale masekeli khumi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akakhala munthu wa zaka zisanu kufikira wina wa zaka makumi awiri uwayesere, wamwamuna wa masekeli makumi awiri, ndi wamkazi wa masekeli khumi.