Leviticus 27:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Akakhala munthu wa mwezi umodzi mpaka zaka zisanu, mtengo wake ukhale wokwana mashekeli asiliva zisanu pa munthu wamwamuna, ndipo zitatu pa munthu wamkazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akakhala mwana wa mwezi umodzi kufikira zaka zisanu, uziwayesera wamwamuna wa masekeli asanu a siliva, ndi wamkazi wa masekeli atatu a siliva.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati ndi munthu wamwamuna wa pakati pa mwezi umodzi ndi zaka zisanu, mtengo wa munthu wamwamuna ukhale masekeli asanu a siliva ndipo ngati ndi wamkazi, ukhale masekeli atatu a siliva.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akakhala mwana wa mwezi umodzi kufikira zaka zisanu, uziwayesera wamwamuna wa masekeli asanu a siliva, ndi wamkazi wa masekeli atatu a siliva.