Leviticus 4:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo aviike chala chake m'magazi, ndi kuwaza magaziwo kasanu ndi kaŵiri patsogolo pa nsalu yochinga malo oyera pamaso pa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo wansembeyo aviike chala chake m'mwazimo, nawaze mwaziwo kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova chakuno cha nsalu yotchinga, ya malo opatulika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye aviyike chala chake mʼmagazi, ndipo awawaze kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova, patsogolo pa katani yotchinga malo wopatulika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo wansembeyo abviike cala cace m'mwazimo, nawaze mwaziwo kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova cakuno ca nsaru yocinga, ya malo opatulika.